Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 83:17 - Buku Lopatulika

17 Achite manyazi, naopsedwe kosatha; ndipo asokonezeke, naonongeke.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Achite manyazi, naopsedwe kosatha; ndipo asokonezeke, naonongeke.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Achitedi manyazi ndi mantha mpaka muyaya, ndipo afe imfa yonyozeka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse; awonongeke mwa manyazi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 83:17
4 Mawu Ofanana  

Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda.


Achite manyazi, nadodome iwo akukondwera chifukwa cha choipa chidandigwera. Avekeke ndi manyazi ndi kupunzika iwo akudzikuza pa ine.


Athe nzeru nachite manyazi iwo akufuna moyo wanga; abwezedwe m'mbuyo nasokonezeke iwo akundipangira chiwembu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa