Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 83:13 - Buku Lopatulika

13 Mulungu wanga, muwaike akhale ngati mungu; ngati ziputu zomka ndi mphepo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Mulungu wanga, muwaike akhale ngati mungu; ngati ziputu zomka ndi mphepo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Inu Mulungu wanga, muŵasandutse ngati fumbi louluka ndi kamvulumvulu, akhale ngati mankhusu ouluka ndi mphepo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga, ngati mankhusu owuluka ndi mphepo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 83:13
15 Mawu Ofanana  

Kodi mudzaopsa tsamba lakungouluka, ndi kulondola ziputu zouma?


Ngati akunga ziputu zomka ndi mphepo, ngati mungu wouluzika ndi nkuntho?


Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji ine? Mukhaliranji kutali kwa chipulumutso changa, ndi kwa mau a kubuula kwanga?


Akhale monga mungu kumphepo, ndipo mngelo wa Yehova awapirikitse.


Inu ndinu mfumu yanga, Mulungu; lamulirani chipulumutso cha Yakobo.


Ndipo ndi ukulu wanu waukulu mwapasula akuukira Inu; mwatumiza mkwiyo wanu, unawanyeketsa ngati chiputu.


Inde sanaokedwe, inde sanafesedwe; inde, muzu wao sunazike pansi; koma Iye anawaombetsera mphepo, ndipo afota, ndipo kamvulumvulu awachotsa monga chiputu.


Ndani anautsa wina wochokera kum'mawa, amene amuitana m'chilungamo, afike pa phazi lake? Iye apereka amitundu patsogolo pake, namlamuliritsa mafumu; nawapereka monga fumbi kulupanga lake, monga chiputu chouluzidwa ku uta wake.


Chifukwa chake ndidzabalalitsa iwo, monga ziputu zakupita, ndi mphepo ya kuchipululu.


Popeza wanena, Mitundu iwiri iyi ya anthu ndi maiko awiri awa adzakhala anga, tidzakhala nao ngati cholowa chathu, angakhale Yehova anali komweko;


Atero Ambuye Yehova, Popeza mdani ananena za inu, Ha! Ingakhale misanje yakale ili yathu, cholowa chathu;


chouluzira chake chili m'dzanja lake, ndipo adzayeretsa padwale pake; ndipo adzasonkhanitsa tirigu wake m'nkhokwe, koma mankhusu adzatentha ndi moto wosazima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa