Masalimo 83:13 - Buku Lopatulika13 Mulungu wanga, muwaike akhale ngati mungu; ngati ziputu zomka ndi mphepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mulungu wanga, muwaike akhale ngati mungu; ngati ziputu zomka ndi mphepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Inu Mulungu wanga, muŵasandutse ngati fumbi louluka ndi kamvulumvulu, akhale ngati mankhusu ouluka ndi mphepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga, ngati mankhusu owuluka ndi mphepo. Onani mutuwo |