Masalimo 83:14 - Buku Lopatulika14 Monga moto upsereza nkhalango, ndi monga lawi liyatsa mapiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Monga moto upsereza nkhalango, ndi monga lawi liyatsa mapiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Monga momwe moto umatenthera nkhalango, monga momwe malaŵi amayakira pa mapiri, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Monga moto umatentha nkhalango, kapena malawi a moto kuyatsa phiri, Onani mutuwo |