Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 81:2 - Buku Lopatulika

2 Utsani salimo, bwera nakoni kalingaka, zeze wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Utsani salimo, bwera nakoni kalingaka, zeze wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Yambani nyimbo, imbani ng'oma, pamodzi ndi pangwe wolira bwino ndi zeze.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Yambani nyimbo, imbani tambolini imbani pangwe wolira bwino ndi zeze.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 81:2
11 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali, pakuchita limodzi amalipenga ndi oimba, kumveketsa mau amodzi akulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi pakukweza mau ao pamodzi ndi malipenga, ndi nsanje, ndi zoimbira zina, ndi kulemekeza Yehova, ndi kuti, Pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake chikhala chikhalire; pamenepo mtambo unadzaza nyumbayi, ndiyo nyumba ya Yehova;


ndi Maaseiya, ndi Semaya, ndi Eleazara, ndi Uzi, ndi Yehohanani, ndi Malikiya, ndi Elamu, ndi Ezere. Ndipo oimbira anaimbitsa Yezeraya ndiye woyang'anira wao.


Ndidzaimbira zakukulemekezani Inu, mphamvu yanga; pakuti Mulungu ndiye msanje wanga, Mulungu wa chifundo changa.


Pa choimbira cha zingwe khumi ndi pachisakasa; pazeze ndi kulira kwake.


Ndipo Miriyamu mneneriyo, mlongo wa Aroni, anagwira lingaka m'dzanja lake; ndipo akazi onse anatuluka kumtsata ndi malingaka ndi kuthira mang'ombe.


Ndipo ataimba nyimbo, anatuluka, namuka kuphiri la Azitona.


ndi kudzilankhulira nokha ndi masalimo, ndi mayamiko, ndi nyimbo zauzimu, kuimbira ndi kuimba m'malimba Ambuye mumtima mwanu;


Mau a Khristu akhalitse mwa inu chichulukire mu nzeru yonse, ndi kuphunzitsa ndi kuyambirirana eni okha ndi masalimo, ndi mayamiko ndi nyimbo zauzimu, ndi kuimbira Mulungu ndi chisomo mumtima mwanu.


Kodi wina wa inu akumva zowawa? Apemphere. Kodi wina asekera? Aimbire.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa