Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 81:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Yambani nyimbo, imbani tambolini imbani pangwe wolira bwino ndi zeze.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Utsani salimo, bwera nakoni kalingaka, zeze wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Utsani salimo, bwera nakoni kalingaka, zeze wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Yambani nyimbo, imbani ng'oma, pamodzi ndi pangwe wolira bwino ndi zeze.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 81:2
11 Mawu Ofanana  

Oyimba malipenga ndi oyimba nyimbo aja amayimba mogwirizana, monga liwu la munthu mmodzi, kutamanda ndi kuyamika Yehova. Mogwirizana ndi malipenga, ziwaya zamalipenga ndi zida zina, anakweza mawu awo motamanda Yehova poyimba kuti, “Yehova ndi wabwino; chikondi chake chikhala mpaka muyaya.” Ndipo Nyumba ya Mulungu wa Yehova inadzaza ndi mtambo,


Panalinso ansembe awa: Maaseya, Semaya, Eliezara, Uzi, Yehohanani, Milikiya, Elamu ndi Ezeri. Gulu loyimba linkatsogozedwa ndi Yezirahayiya.


Inu mphamvu yanga, ndiyimba matamando kwa inu; Inu Mulungu, ndinu linga langa, Mulungu wanga wachikondi.


kuyimbira nyimbo choyimbira cha zingwe khumi ndi mayimbidwe abwino a zeze.


Ndipo Miriamu mneneri wamkazi, mlongo wa Aaroni anatenga zoyimbira ndipo akazi onse anamutsatira pambuyo, akuyimba ndi zoyimbira ndi kuvina.


Atayimba nyimbo, anapita ku phiri la Olivi.


Muziyankhulana wina ndi mnzake mawu a Masalimo, nyimbo za Mulungu ndi nyimbo za uzimu. Muziyimbira Ambuye movomerezana ndi mitima yanu.


Mawu a Khristu akhazikike kwathunthu mʼmitima mwanu. Muziphunzitsana ndi kulangizana wina ndi mnzake ndi nzeru zonse pamene mukuyimba Masalimo, nyimbo zotamanda ndi nyimbo zauzimu, kuyimbira Mulungu ndi mitima yoyamika.


Kodi alipo wina mwa inu amene ali pa mavuto? Apemphere. Kodi wina wakondwa? Ayimbe nyimbo zolemekeza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa