Masalimo 76:6 - Buku Lopatulika6 Pa kudzudzula kwanu, Mulungu wa Yakobo, galeta ndi kavalo yemwe anagwa m'tulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pa kudzudzula kwanu, Mulungu wa Yakobo, galeta ndi kavalo yemwe anagwa m'tulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamene mudaŵaopsa, Inu Mulungu wa Yakobe, onse okwera pa akavalo ndi akavalo ao omwe adagwa nangoti kakasi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo, kavalo pamodzi ndi galeta zimakhala chete zitagona pansi. Onani mutuwo |