Masalimo 76:12 - Buku Lopatulika12 Iye adzadula mzimu wa akulu; akhala woopsa kwa mafumu a padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Iye adzadula mzimu wa akulu; akhala woopsa kwa mafumu a pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 ndiye amene amathetsa mphamvu akalonga ndipo amaopsa mafumu a pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iye amaswa mzimu wa olamulira; amaopedwa ndi mafumu a dziko lapansi. Onani mutuwo |