Masalimo 72:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo adzachita ufumu kuchokera kunyanja kufikira kunyanja, ndi kuchokera ku Mtsinje kufikira malekezero a dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo adzachita ufumu kuchokera kunyanja kufikira kunyanja, ndi kuchokera ku Mtsinje kufikira malekezero a dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Idzakhala ikulamulira kuchokera ku nyanja ina mpaka ku nyanja ina, kuchokeranso ku Mtsinje mpaka ku mathero a dziko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iye adzalamulira kuchokera ku nyanja ina mpaka ku nyanja ina ndiponso kuchokera ku mtsinje mpaka ku malekezero a dziko lapansi. Onani mutuwo |