Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 72:6 - Buku Lopatulika

6 Adzanga mvula yakugwa pa udzu wosenga, monga mvula yothirira dziko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Adzanga mvula yakugwa pa udzu wosenga, monga mvula yothirira dziko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Idzakhala madalitso ngati mvula yogwa pa minda ngati mvula yowaza pa nthaka!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Iye adzakhala kugwa kwa mvula pa minda yolimidwa ngati mivumbi yothirira dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 72:6
11 Mawu Ofanana  

Iye adzakhala ngati kuunika kwa m'mawa, potuluka dzuwa, M'mawa mopanda mitambo; pamene msipu uphuka kutuluka pansi, chifukwa cha kuwala koyera, italeka mvula.


Mukhutitsa nthaka yake yolima; mufafaniza nthumbira zake; muiolowetsa ndi mvumbi; mudalitsa mmera wake.


M'kuunika kwa nkhope ya mfumu muli moyo; kukoma mtima kwake kunga mtambo wa mvula ya masika.


Mkwiyo wa mfumu ukunga kubangula kwa mkango; koma kukoma mtima kwake kunga mame pamsipu.


ndipo ndidzaupasula; sudzadzomboleredwa kapena kulimidwa; koma padzamera lunguzi ndi minga; ndidzalamuliranso mitambo kuti isavumbwepo mvula.


Tidziwe tsono, tilondole kudziwa Yehova; kutuluka kwake kwakonzekeratu ngati matanda kucha; ndipo adzatidzera ngati mvula, ngati mvula ya masika yakuthirira dziko.


Ndipo iwo adzatha dziko la Asiriya ndi lupanga, ndi dziko la Nimirodi, ndilo polowera pake; ndipo adzatilanditsa kwa a ku Asiriya pamene alowa m'dziko lathu, pamene aponda m'kati mwa malire athu.


Chiphunzitso changa chikhale ngati mvula; maneno anga agwe ngati mame; ngati mvula yowaza pamsipu, ndi monga madontho a mvula pazitsamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa