Masalimo 72:6 - Buku Lopatulika6 Adzanga mvula yakugwa pa udzu wosenga, monga mvula yothirira dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Adzanga mvula yakugwa pa udzu wosenga, monga mvula yothirira dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Idzakhala madalitso ngati mvula yogwa pa minda ngati mvula yowaza pa nthaka! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye adzakhala kugwa kwa mvula pa minda yolimidwa ngati mivumbi yothirira dziko lapansi. Onani mutuwo |