Masalimo 72:5 - Buku Lopatulika5 Adzakuopani momwe likhalira dzuwa ndi mwezi, kufikira mibadwomibadwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Adzakuopani momwe likhalira dzuwa ndi mwezi, kufikira mibadwomibadwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Idzakhala moyo pa mibadwo yonse, nthaŵi zonse pamene dzuŵa ndi mwezi zikuŵala mu mlengalenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Adzakhala ndi moyo pa mibado yonse, nthawi zonse pamene dzuwa ndi mwezi zikuwala. Onani mutuwo |