Masalimo 72:12 - Buku Lopatulika12 Pakuti adzapulumutsa waumphawi wofuulayo; ndi wozunzika amene alibe mthandizi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pakuti adzapulumutsa waumphawi wofuulayo; ndi wozunzika amene alibe mthandizi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndithu iyo idzalanditsa anthu osoŵa amene amaiitana, idzapulumutsa anthu osauka ndiponso opanda woŵathandiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pakuti iye adzawombola wosowa amene akulira, wozunzika amene alibe wina womuthandiza. Onani mutuwo |