Masalimo 72:11 - Buku Lopatulika11 Inde mafumu onse adzamgwadira iye, amitundu onse adzamtumikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Inde mafumu onse adzamgwadira iye, amitundu onse adzamtumikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mafumu onse adzaigwadira ndipo mitundu yonse ya anthu idzaitumikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mafumu onse adzamuweramira ndipo mitundu yonse idzamutumikira. Onani mutuwo |