Masalimo 7:3 - Buku Lopatulika3 Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita ichi; ngati m'manja anga muli chosalungama; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita ichi; ngati m'manja anga muli chosalungama; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chauta Mulungu wanga, ngati ndachita izi: kumchimwira munthu aliyense, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Inu Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita izi ndipo ndapezeka wolakwa, Onani mutuwo |