Masalimo 7:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Inu Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita izi ndipo ndapezeka wolakwa, Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita ichi; ngati m'manja anga muli chosalungama; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yehova Mulungu wanga, ngati ndachita ichi; ngati m'manja anga muli chosalungama; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chauta Mulungu wanga, ngati ndachita izi: kumchimwira munthu aliyense, Onani mutuwo |
Tsono abambo anga, onanitu kansalu ka mkanjo wanu kali mʼdzanja langali! Popeza kuti ndinatha kudula msonga ya mkanjo wanu koma osakuphani, pamenepo mudziwe kuti ine ndilibe maganizo woti ndikuchiteni choyipa kapena kukuwukirani. Sindinakulakwireni ngakhale kuti inu mukufuna moyo wanga kuti mundiphe.