Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 7:2 - Buku Lopatulika

2 kuti angamwetule moyo wanga ngati mkango, ndi kuukadzula, wopanda wina wondilanditsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 kuti angamwetule moyo wanga ngati mkango, ndi kuukadzula, wopanda wina wondilanditsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 kuti iwo anganding'ambe ngati mkango, ndi kundikadzula popanda wina wondipulumutsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 mwina angandikadzule ngati mkango, ndi kundingʼamba popanda wondipulumutsa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 7:2
18 Mawu Ofanana  

Ndipo mdzakazi wanu ndinali nao ana aamuna awiri, ndipo awiriwo analimbana kumunda, panalibe wina wakuwaletsa, koma wina anakantha mnzake namupha.


chinkana mudziwa kuti sindili woipa, ndipo palibe wakupulumutsa m'dzanja lanu?


Alalira monga mkango m'ngaka mwake; alalira kugwira wozunzika, agwira wozunzika, pakumkola mu ukonde mwake.


Ndakhulupirira Yehova, mutani nkunena kwa moyo wanga, Thawirani kuphiri lanu ngati mbalame?


Ndisungeni ine, Mulungu: pakuti ndakhulupirira Inu.


Afanana ndi mkango wofuna kumwetula, ndi msona wa mkango wakukhala mobisalamo.


Andiyasamira m'kamwa mwao, ngati mkango wozomola ndi wobangula.


Munditcherere khutu lanu; ndipulumutseni msanga. Mundikhalire ine thanthwe lolimba, nyumba yamalinga yakundisunga.


Ndipo pakutsimphina ine anakondwera, nasonkhana pamodzi; akundipanda anandisonkhanira; ndipo sindinachidziwe, ananding'amba osaleka.


Dziwitsani ichi inu oiwala Mulungu, kuti ndingakumwetuleni, ndipo mungasowepo mpulumutsi.


Mundilanditse kwa ochita zopanda pake, ndipo ndipulumutseni kwa anthu olira mwazi.


Mkwiyo wa mfumu ukunga kubangula kwa mkango; koma kukoma mtima kwake kunga mame pamsipu.


Ndinadzitonthoza kufikira mamawa; monga mkango, momwemo Iye anathyolathyola mafupa anga onse; Kuyambira usana kufikira usiku mudzanditsiriza ine.


Ndi za Gadi anati, Wodala iye amene akuza Gadi; akhala ngati mkango waukazi, namwetula dzanja, ndi pakati pamutu pomwe.


Koma Ambuye anaima nane nandipatsa mphamvu; kuti mwa ine chilalikiro chimveke konsekonse, ndi amitundu onse amve; ndipo ndinalanditsidwa m'kamwa mwa mkango.


Khalani odzisungira, dikirani; mdani wanu mdierekezi, monga mkango wobuma, ayendayenda ndi kufunafuna wina akamlikwire:


Ndipo panalibe wolanditsa, popeza ku Sidoni nkutali, ndipo analibe kuyenderana ndi anthu ena; ndiko ku chigwa chokhala ku Beterehobu. Pamenepo anamanganso mzindawo, nakhala m'mwemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa