Masalimo 7:2 - Buku Lopatulika2 kuti angamwetule moyo wanga ngati mkango, ndi kuukadzula, wopanda wina wondilanditsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 kuti angamwetule moyo wanga ngati mkango, ndi kuukadzula, wopanda wina wondilanditsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 kuti iwo anganding'ambe ngati mkango, ndi kundikadzula popanda wina wondipulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 mwina angandikadzule ngati mkango, ndi kundingʼamba popanda wondipulumutsa. Onani mutuwo |