Masalimo 7:1 - Buku Lopatulika1 Yehova Mulungu wanga, ndakhulupirira Inu; mundipulumutse kwa onse akundilonda, nimundilanditse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova Mulungu wanga, ndakhulupirira Inu; mundipulumutse kwa onse akundilonda, nimundilanditse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta, Mulungu wanga, ndikuthaŵira kwa Inu. Mundilanditse kwa onse ondithamangitsa. Mundipulumutse, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Yehova Mulungu wanga, Ine ndikuthawira kwa Inu; pulumutseni ndi kundilanditsa kwa onse amene akundithamangitsa, Onani mutuwo |