Masalimo 7:4 - Buku Lopatulika4 ngati ndambwezera choipa iye woyanjana ndine; (inde, ndamlanditsa wondisautsa kopanda chifukwa); Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ngati ndambwezera choipa iye woyanjana ndine; (inde, ndamlanditsa wondisautsa kopanda chifukwa); Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 kubwezera choipa bwenzi langa, kapena kumulanda zinthu mdani wanga popanda chifukwa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 ngati ndachita zoyipa kwa iye amene ndili naye pa mtendere, kapena popanda chifukwa ndalanda mdani wanga, Onani mutuwo |