Masalimo 69:3 - Buku Lopatulika3 Ndalema ndi kufuula kwanga; kum'mero kwauma gwaa! M'maso mwanga mwada poyembekeza Mulungu wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndalema ndi kufuula kwanga; kum'mero kwauma gwa! M'maso mwanga mwada poyembekeza Mulungu wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndafooka ndi kulira kwanga, kum'mero kwanga kwauma. M'maso mwada pamene ndikuyembekezera Mulungu wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndafowoka ndikupempha chithandizo; kummero kwanga kwawuma gwaa, mʼmaso mwanga mwada kuyembekezera Mulungu wanga. Onani mutuwo |