Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 67:5 - Buku Lopatulika

5 Anthu akuyamikeni, Mulungu; anthu onse akuyamikeni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Anthu akuyamikeni, Mulungu; anthu onse akuyamikeni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Mitundu yonse ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu, mitundu yonse ya anthu ikuyamikeni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu; mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 67:5
4 Mawu Ofanana  

Anthu akuyamikeni, Mulungu; anthu onse akuyamikeni.


Ndipo Yehova adzakhala msanje kwa iye wokhalira mphanthi. Msanje m'nyengo za nsautso;


Ndipo kudzatero, ukamuka nafe, inde, kudzali kuti zokoma zilizonse Yehova atichitira ife, zomwezo tidzakuchitira iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa