Masalimo 64:8 - Buku Lopatulika8 Adzawakhumudwitsa, lilime lao lidzawatsutsa; onse akuwaona adzawathawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Adzawakhumudwitsa, lilime lao lidzawatsutsa; onse akuwaona adzawathawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Adzaŵaononga chifukwa cha zokamba zao, onse oŵapenya adzapukusa mitu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iye adzatembenuza milomo yawoyo kuwatsutsa ndi kuwasandutsa bwinja; onse amene adzawaona adzagwedeza mitu yawo mowanyoza. Onani mutuwo |