Masalimo 64:6 - Buku Lopatulika6 Afunafuna zosalungama; kusanthula, asanthuladi mpaka kutha; chingakhale cha m'kati mwake mwa munthu, ndi mtima wozama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Afunafuna zosalungama; kusanthula, asanthuladi mpaka kutha; chingakhale cha m'kati mwake mwa munthu, ndi mtima wozama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Amaganizira zoipa nkumati, “Takonza mochenjera ndithu chiwembu chathu.” Malingaliro ndi zofuna za mtima wa munthu nzobisika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwo amakonzekera zosalungama ndipo amati, “Takonza ndondomeko yabwino kwambiri!” Ndithu maganizo ndi mtima wa munthu ndi zachinyengo. Onani mutuwo |