Masalimo 64:10 - Buku Lopatulika10 Wolungama adzakondwera mwa Yehova, nadzakhulupirira Iye; ndipo oongoka mtima onse adzalemekeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Wolungama adzakondwera mwa Yehova, nadzakhulupirira Iye; ndipo oongoka mtima onse adzalemekeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chauta adalitse anthu ake mtendere ndi chimwemwe zikhale nao, anthu akondwere chifukwa cha Chauta Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Lolani wolungama akondwere mwa Yehova ndi kubisala mwa Iye, owongoka mtima onse atamande Iye! Onani mutuwo |