Masalimo 61:7 - Buku Lopatulika7 Adzakhala nthawi zonse pamaso pa Mulungu; mumpatse chifundo ndi choonadi zimsunge. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Adzakhala nthawi zonse pamaso pa Mulungu; mumpatse chifundo ndi choonadi zimsunge. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Akhale pa mpando wake waufumu pamaso pa Mulungu mpaka muyaya. Inu Chauta, mumsunge mokhulupirika chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya; ikani chikondi chanu ndi kukhulupirika kwanu kuti zimuteteze. Onani mutuwo |