Masalimo 60:9 - Buku Lopatulika9 Adzandifikitsa ndani m'mzinda wa m'linga? Adzanditsogolera ndani ku Edomu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Adzandifikitsa ndani m'mudzi wa m'linga? Adzanditsogolera ndani ku Edomu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndani adzandifikitse ku mzinda wamalinga? Ndani adzanditsogolere ku Edomu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu? Onani mutuwo |