Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 60:10 - Buku Lopatulika

10 Si ndinu, Mulungu, amene mwatitaya? Osatuluka nao makamu athu, Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Si ndinu, Mulungu, amene mwatitaya? Osatuluka nao makamu athu, Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Si wina ai koma ndinu Mulungu amene mwatitaya, ndinu Mulungu amene mwaleka kuperekeza ankhondo athu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife ndipo simutuluka pamodzi ndi magulu athu ankhondo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 60:10
17 Mawu Ofanana  

Ndipo anakantha Amowabu nawayesa ndi chingwe, nawagonetsa pansi; ndipo anawayesera zingwe ziwiri kupha, ndi chingwe chimodzi chathunthu kusunga ndi moyo. Ndipo Amowabu anakhala anthu a Davide, nabwera nayo mitulo.


Pamenepo Davide anaika maboma mu Aramu wa Damasiko. Ndipo Aaramu anasanduka anthu a Davide, nabwera nayo mitulo. Ndipo Yehova anamsunga Davide kulikonse anamukako.


Si ndinu Mulungu, amene mwatitaya osatuluka nao magulu athu?


Ena atama magaleta, ndi ena akavalo; koma ife tidzatchula dzina la Yehova Mulungu wathu.


Mwatitaya Mulungu, mwatipasula; mwakwiya; tibwezereni.


Ndipo ndidzalindira Yehova, amene wabisira a nyumba ya Yakobo nkhope yake, ndipo ndidzamyembekeza Iye.


Koma Yehova anati kwa ine, Nena nao, Musakwerako, kapena kuthira nkhondo; popeza sindili pakati panu; angakukantheni adani anu.


pakuti Yehova Mulungu wanu ndiye wakumuka nanu, kugwirira inu pa adani anu, kukupulumutsani.


Ndipo Yoswa anagwira mafumu awa onse ndi dziko lao nthawi yomweyi; chifukwa Yehova Mulungu wa Israele anathirira Israele nkhondo.


Mwa ichi ana a Israele sangathe kuima pamaso pa adani ao, awafulatira adani ao, pakuti aperekedwa aonongeke. Sindidzakhalanso nanu mukapanda kuononga choperekedwacho, kuchichotsa pakati pa inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa