Masalimo 60:11 - Buku Lopatulika11 Tithandizeni kunsautso; kuti chipulumutso cha munthu ndi chabe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Tithandizeni kunsautso; kuti chipulumutso cha munthu ndi chabe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tithandizeni kulimbana ndi adani athuwo, pakuti chithandizo cha munthu nchopandapake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu, pakuti thandizo lochokera kwa munthu ndi lopanda phindu. Onani mutuwo |