Masalimo 60:2 - Buku Lopatulika2 Mwagwedeza dziko, mwaling'amba. Konzani ming'alu yake; pakuti ligwedezeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mwagwedeza dziko, mwaling'amba. Konzani ming'alu yake; pakuti ligwedezeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Inu mwagwedeza dziko ndi chivomezi, Inu mwaling'amba. Konzani ming'alu yake, pakuti likugwedezeka koopsa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba, konzani mingʼalu yake pakuti ikugwedezeka kwambiri. Onani mutuwo |