Masalimo 57:9 - Buku Lopatulika9 Ndidzakuyamikirani mwa anthu, Ambuye, ndidzakuimbirani mwa mitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndidzakuyamikirani mwa anthu, Ambuye, ndidzakuimbirani mwa mitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndidzakuthokozani, Inu Chauta, pakati pa mitundu ya anthu. Ndidzaimba nyimbo zokutamandani pakati pa anthu a maiko onse, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu, ndidzayimba za Inu pakati pa mayiko. Onani mutuwo |