Masalimo 57:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti chifundo chanu nchachikulu kufikira m'mwamba, ndi choonadi chanu kufikira mitambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti chifundo chanu nchachikulu kufikira m'mwamba, ndi choonadi chanu kufikira mitambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 pakuti chikondi chanu chosasinthika nchachikulu, chofika mpaka mlengalenga, kukhulupirika kwanu kumafika mpaka ku mitambo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba; kukhulupirika kwanu kwafika ku mitambo. Onani mutuwo |