Masalimo 57:6 - Buku Lopatulika6 Ananditchera ukonde apo ndiyenda; moyo wanga wawerama. Anandikumbira mbuna patsogolo panga; anagwa m'kati mwake iwo okha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ananditchera ukonde apo ndiyenda; moyo wanga wawerama. Anandikumbira mbuna patsogolo panga; anagwa m'kati mwake iwo okha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Iwo aja adatchera mapazi anga ukonde. Mtima wanga umavutika kwambiri. Akumba mbuna m'njira yanga, koma agweramo okha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwo anatchera mapazi anga ukonde ndipo ndinawerama pansi mosautsidwa. Anakumba dzenje mʼnjira yanga koma agweramo okha mʼmenemo. Onani mutuwo |