Masalimo 57:5 - Buku Lopatulika5 Mukwezeke m'mwambamwamba, Mulungu; ulemerero wanu ukhale pamwamba padziko lonse lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mukwezeke m'mwambamwamba, Mulungu; ulemerero wanu ukhale pamwamba pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Inu Mulungu, onetsani ukulu wanu kumwambamwamba, wanditsani ulemerero wanu pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba; mulole kuti ulemerero wanu ukhale pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwo |