Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 54:3 - Buku Lopatulika

3 Pakuti alendo andiukira, ndipo oopsa afunafuna moyo wanga; sadziikira Mulungu pamaso pao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Pakuti alendo andiukira, ndipo oopsa afunafuna moyo wanga; sadziikira Mulungu pamaso pao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Anthu onyada andiwukira, anthu ankhalwe amafunafuna moyo wanga, iwo saganizako za Inu Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Alendo akundithira nkhondo; anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga, anthu amene salabadira za Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 54:3
13 Mawu Ofanana  

Ndaika Yehova patsogolo panga nthawi zonse; popeza ali padzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.


likutumizire thandizo lotuluka m'malo oyera, ndipo likugwirizize kuchokera mu Ziyoni;


Pakuti andizinga agalu, msonkhano wa oipa wanditsekereza; andiboola m'manja anga ndi m'mapazi anga.


Cholakwa cha woipayo chimati m'kati mwa mtima wanga, palibe kuopa Mulungu pamaso pake.


Achite manyazi nadodome iwo akulondola moyo wanga kuti auononge. Abwerere m'mbuyo, nachite manyazi iwo okondwera kundichitira choipa.


Mundiweruzire, Mulungu, ndipo mundinenere mlandu kwa anthu opanda chifundo. Mundilanditse kwa munthu wonyenga ndi wosalungama.


Kodi ochita zopanda pake sadziwa? Pomadya anthu anga monga akudya mkate; ndipo saitana Mulungu.


Abale anga andiyesa mlendo, ndi ana a mai wanga andiyesa wa mtundu wina.


Mulungu, odzikuza andiukira, ndi msonkhano wa anthu oopsa afuna moyo wanga, ndipo sanaike Inu pamaso pao.


Ndipo izi adzachita, chifukwa sanadziwe Atate, kapena Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa