Masalimo 54:4 - Buku Lopatulika4 Taonani, Mulungu ndiye mthandizi wanga, Ambuye ndiye wachirikiza moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Taonani, Mulungu ndiye mthandizi wanga, Ambuye ndiye wachirikiza moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Komatu, Mulungu ndiye amandithandiza, Ambuye ndiwo amachirikiza moyo wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa; Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine. Onani mutuwo |