Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 54:4 - Buku Lopatulika

4 Taonani, Mulungu ndiye mthandizi wanga, Ambuye ndiye wachirikiza moyo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Taonani, Mulungu ndiye mthandizi wanga, Ambuye ndiye wachirikiza moyo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Komatu, Mulungu ndiye amandithandiza, Ambuye ndiwo amachirikiza moyo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa; Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 54:4
10 Mawu Ofanana  

Pamenepo mzimu unavala Amasai, ndiye wamkulu wa makumi atatuwo, nati iye, Ndife anu, Davide, tivomerezana nanu mwana wa Yese inu: mtendere, mtendere ukhale ndi inu, ndi mtendere ukhale ndi athandizi anu; pakuti Mulungu wanu akuthandizani. Ndipo Davide anawalandira, nawaika akulu a magulu.


Kundikankha anandikankha ndikadagwa; koma Yehova anandithandiza.


Yehova, imvani chilungamo, mverani mfuu wanga; tcherani khutu ku pemphero langa losatuluka m'milomo ya chinyengo.


Ndipo ine, mundigwirizize mu ungwiro wanga, ndipo mundiike pankhope panu kunthawi yamuyaya.


usaope, pakuti Ine ndili pamodzi ndi iwe; usaopsedwe, pakuti Ine ndine Mulungu wako; ndidzakulimbitsa; inde, ndidzakuthangata; inde, ndidzakuchirikiza ndi dzanja langa lamanja la chilungamo.


Taona Mtumiki wanga, amene ndimgwiriziza; Wosankhika wanga, amene moyo wanga ukondwera naye; ndaika mzimu wanga pa Iye; Iye adzatulutsira amitundu chiweruziro.


Ndipo tidzatani ndi zinthu izi? Ngati Mulungu ali ndi ife, adzatikaniza ndani?


Kotero kuti tinena molimbika mtima, Mthandizi wanga ndiye Ambuye; sindidzaopa; adzandichitira chiyani munthu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa