Masalimo 54:1 - Buku Lopatulika1 Ndipulumutseni, Mulungu, mwa dzina lanu, ndipo mundiweruze ndi mphamvu yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipulumutseni, Mulungu, mwa dzina lanu, ndipo mundiweruze ndi mphamvu yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Mulungu, pulumutseni ndi dzina lanu, onetsani ndi mphamvu zanu kuti ndine wosalakwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu; onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu. Onani mutuwo |