Masalimo 53:6 - Buku Lopatulika6 Ha, chipulumutso cha Israele chichokere mu Ziyoni! Pakubweretsa Mulungu anthu ake a m'ndende, Yakobo adzakondwera, Israele adzasekera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ha, chipulumutso cha Israele chichokere m'Ziyoni! Pakubweretsa Mulungu anthu ake a m'ndende, Yakobo adzakondwera, Israele adzasekera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chibwere ndithu chipulumutso cha Israele kuchokera ku Ziyoni! Mulungu akadzaŵabwezera ufulu anthu ake, Yakobe adzakondwera, Israele adzasangalala kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndithu, chipulumutso cha Israeli nʼchochokera ku Ziyoni! Pamene Mulungu adzabwezeretsanso ulemerero wa anthu ake, lolani Yakobo akondwere ndi Israeli asangalale! Onani mutuwo |