Masalimo 45:10 - Buku Lopatulika10 Tamvera, mwana wamkaziwe, taona, tatchera khutu lako; uiwalenso mtundu wako ndi nyumba ya atate wako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Tamvera, mwana wamkaziwe, taona, tatchera khutu lako; uiwalenso mtundu wako ndi nyumba ya atate wako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono mvera kuno, mkwati wamkaziwe, imva mau anga ndipo uŵaganizire bwino. Iŵala abale ako ndiponso nyumba ya bambo wako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Tamvera, iwe mwana wa mkazi ganizira ndipo tchera khutu; iwala anthu ako ndi nyumba ya abambo ako. Onani mutuwo |