Masalimo 45:9 - Buku Lopatulika9 Mwa omveka anu muli ana aakazi a mafumu; ku dzanja lanu lamanja aima mkazi wa mfumu wovala golide wa ku Ofiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mwa omveka anu muli ana akazi a mafumu; ku dzanja lanu lamanja aima mkazi wa mfumu wovala golide wa ku Ofiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 ana aakazi a mafumu ali m'gulu la mbumba zanu zolemekezeka. Ku dzanja lanu lamanja kwaima mfumukazi, yovala zovala za golide wa ku Ofiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ana aakazi a mafumu ali pakati pa akazi anu olemekezeka; ku dzanja lanu lamanja kuli mkwatibwi waufumu ali mu golide wa ku Ofiri. Onani mutuwo |