Masalimo 45:8 - Buku Lopatulika8 Zovala zanu zonse nza mure, ndi khonje, ndi kasiya; m'zinyumba za mfumu zomanga ndi minyanga ya njovu mwatuluka zoimba za zingwe zokukondweretsani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Zovala zanu zonse nza mure, ndi khonje, ndi kasiya; m'zinyumba za mfumu zomanga ndi minyanga ya njovu mwatuluka zoimba za zingwe zokukondweretsani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Zovala zanu nzonunkhira mure, aloe ndi kasiya. Nyumba zanu zachifumu nzomangidwa ndi mnyanga. M'menemo zoimbira zansambo zimakusangalatsani, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mikanjo yanu yonse ndi yonunkhira ndi mure ndi aloe ndi kasiya; kuchokera ku nyumba zaufumu zokongoletsedwa ndi mnyanga wanjovu nyimbo za zoyimbira zazingwe zimakusangalatsani. Onani mutuwo |