Masalimo 36:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti chitsime cha moyo chili ndi Inu, M'kuunika kwanu tidzaona kuunika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti chitsime cha moyo chili ndi Inu, M'kuunika kwanu tidzaona kuunika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kwa Inu kuli kasupe wamoyodi, m'kuŵala kwanu ifenso timaona kuŵala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo; mʼkuwala kwanu ifenso timaona kuwala. Onani mutuwo |