Masalimo 36:8 - Buku Lopatulika8 Adzakhuta kwambiri ndi zonona za m'nyumba mwanu, ndipo mudzawamwetsa mu mtsinje wa zokondweretsa zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Adzakhuta kwambiri ndi zonona za m'nyumba mwanu, ndipo mudzawamwetsa mu mtsinje wa zokondweretsa zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mumaŵadyetsa zonona m'nyumba mwanu, ndipo mumaŵamwetsa madzi a mu mtsinje wa madalitso anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu; Inu mumawapatsa chakumwa kuchokera mu mtsinje wanu wachikondwerero. Onani mutuwo |