Masalimo 32:11 - Buku Lopatulika11 Sekerani mwa Yehova, ndimo kondwerani inu olungama mtima; ndipo fuulani mokondwera nonsenu oongoka mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Sekerani mwa Yehova, ndimo kondwerani inu olungama mtima; ndipo fuulani mokondwera nonsenu oongoka mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Sangalalani ndi kukondwa inu nonse okonda Mulungu, chifukwa cha zimene Chautayo adakuchitirani. Inu anthu ake onse, fuulani ndi chimwemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kondwerani mwa Yehova inu olungama; imbani, inu nonse amene muli owongoka mtima! Onani mutuwo |