Masalimo 32:10 - Buku Lopatulika10 Zisoni zambiri zigwera woipa; koma chifundo chidzamzinga iye wakukhulupirira Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Zisoni zambiri zigwera woipa; koma chifundo chidzamzinga iye wakukhulupirira Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Anthu oipa amapeza zoŵaŵa zambiri, koma munthu wokhulupirira Chauta amazingidwa ndi chikondi chosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Zowawa ndi zambiri za anthu oyipa koma chikondi chosatha cha Yehova chimamuzinga munthu amene amadalira Iye. Onani mutuwo |