Masalimo 33:1 - Buku Lopatulika1 Fuulani mokondwera mwa Yehova, inu olungama mtima, oongoka mtima ayenera kulemekeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Fuulani mokondwera mwa Yehova, inu olungama mtima, oongoka mtima ayenera kulemekeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Kondwerani mwa Chauta, inu anthu ake. Zoonadi ochita zolungama azitamanda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Imbirani Yehova mokondwera Inu olungama, nʼkoyenera kuti owongoka mtima azitamanda Iyeyo. Onani mutuwo |