Masalimo 33:2 - Buku Lopatulika2 Yamikani Yehova ndi zeze; muimbireni ndi chisakasa cha zingwe khumi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yamikani Yehova ndi zeze; muimbireni ndi chisakasa cha zingwe khumi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tamandani Chauta ndi pangwe. Muimbireni nyimbo ndi zeze wa nsambo khumi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mutamandeni Yehova ndi pangwe; muyimbireni Iye nyimbo pa zeze wa zingwe khumi. Onani mutuwo |