Masalimo 33:3 - Buku Lopatulika3 Mumuimbire Iye nyimbo yatsopano; muimbe mwaluso kumveketsa mau. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mumuimbire Iye nyimbo yatsopano; muimbe mwaluso kumveketsa mau. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Muimbireni nyimbo yatsopano, kodolani nsambozo mwaluso ndi kufuula mosangalala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Muyimbireni nyimbo yatsopano; imbani mwaluso, ndipo fuwulani mwachimwemwe. Onani mutuwo |