Masalimo 33:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti mau a Yehova ali olunjika; ndi ntchito zake zonse zikhulupirika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti mau a Yehova ali olunjika; ndi ntchito zake zonse zikhulupirika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mau a Chauta ndi olungama, zochita zake zonse amazichita mokhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pakuti mawu a Yehova ndi olungama ndi owona; Iye ndi wokhulupirika pa zonse zimene amachita. Onani mutuwo |