Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 28:6 - Buku Lopatulika

6 Wodalitsika Yehova, Pakuti adamva mau a kupemba kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Wodalitsika Yehova, Pakuti adamva mau a kupemba kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Chauta atamandike, pakuti wamva liwu la kupempha kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Matamando apite kwa Yehova, popeza Iye wamva kupempha chifundo kwanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 28:6
6 Mawu Ofanana  

M'mene ndinasautsika ndinaitanira pa Yehova; anandiyankha nandiika motakasuka Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa