Masalimo 28:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti sasamala ntchito za Yehova, kapena machitidwe a manja ake, adzawapasula, osawamanganso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti sasamala ntchito za Yehova, kapena machitidwe a manja ake, adzawapasula, osawamanganso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chifukwa chakuti iwo sasamalako ntchito za Chauta, ngakhale zimene adalenga Iye. Chauta adzaŵagumula ngati nyumba, osaŵamanganso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Popeza iwowo sakhudzidwa ndi ntchito za Yehova, ndi zimene manja ake anazichita, Iye adzawakhadzula ndipo sadzawathandizanso. Onani mutuwo |
Ndipo kudzakhala kuti ukadzamvera iwe zonse ndikulamulirazo, nukadzayenda m'njira zanga ndi kuchita chilungamo pamaso panga, kusunga malemba anga ndi malamulo anga, monga anatero Davide mtumiki wanga pamenepo Ine ndidzakhala ndi iwe, ndidzakumangira ndi kukukhazikitsira nyumba, monga ndinammangira Davide, ndipo ndidzakupatsa iwe Israele.