Masalimo 26:9 - Buku Lopatulika9 Musandichotsere mzimu wanga pamodzi ndi olakwa, kapena moyo wanga pamodzi ndi anthu okhetsa mwazi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Musandichotsere mzimu wanga pamodzi ndi olakwa, kapena moyo wanga pamodzi ndi anthu okhetsa mwazi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Musanditayire kumodzi ndi anthu ochimwa, musandichotsere moyo pamodzi ndi anthu ofuna kupha anzao, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa, moyo wanga pamodzi ndi anthu akupha anzawo, Onani mutuwo |