Masalimo 26:10 - Buku Lopatulika10 amene m'manja mwao muli mphulupulu, ndi dzanja lao lamanja ladzala ndi zokometsera mlandu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 amene m'manja mwao muli mphulupulu, ndi dzanja lao lamanja ladzala ndi zokometsera mlandu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 anthu amene manja ao amachita zoipa, ndipo anthu amene dzanja lao lamanja ndi lodzaza ndi ziphuphu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa, dzanja lawo lamanja ladzaza ndi ziphuphu. Onani mutuwo |